Commandments Devotions

Lamulo Lachisanu Ndi Chinayi (9): Usamnamizire Mnzako

Eksodo 20:16

Mawu Otsogolera

Lero tipitiriza kukambirana za Malamulo khumi monga takhalatikuchitira m’miyezi iwiri yapitayi. Lerotikambirana pa za lamulo lachisanu ndi chinayi. Koma tisanayang’ane lamuloli tiyeni tione mfundo izi za malamulo khumi onse.

  1. Malamulo khumi anali mawu amene anachita kuchokera kwa mwini Mulungu. Sakuyener...

    Read more

     

Lamulo Lachisanu Ndi Chitatu (8): Usabe

Mawu Otsogolera

Mulungu anapanga malamulo kuti munthu ndi zolengedwa zina zonse zipindule. Chinthu chilichonse chomwe Mulungu anachilenga chimachitika ndi chikonzero cha Mulungu mwini ndipo pakakhala kusemphana ndi chikonzerochi zinthuzo zimaonongeka. Mwachitsanzo, nsomba zinalengedwa kuti zizikhala m’madzi. Ndi chifukwa chake zikakhala pamtunda zimafa. Dzuwa limatulikira kum’mawa ndi kukolowera kum...

Read more

 

The Ten Commandments - Knowing The Only True God

Bible Readings:

Psalm 24:1-10, Exodus 20:1-21 & Matthew 22: 34-40

‌Today we are laying a foundation on the sub-theme for the first half of 2022, which is “Knowing God”, derived from John 17:3 And this is life eternal, that they might know thee the only true God, and Jesus Christ, whom thou hast sent. As such, in the first part of this year, we will be expounding on the Ten Commandments...

Read more

 


About Us

Zomba CCAP congregation, located in Zomba City, the old capital of Malawi, was established in 1898, and currently boasts 1,638 Christians, of which 115 are church elders and 103 church deacons. It has vibrant women and youth ministries, and a management team that co-ordinates the work of eleven committees, among which are the partnership, evangelism and intercessory, and music committee, as well as faith and works committee... Read more

Announcements & Events

Explosion 2023 Posted: 13 Apr, 2023
Zomba CCAP Holy Week Time Table Posted: 3 Apr, 2023

Address

Zomba C.C.A.P.
Chimbiya Road
P.O. Box 355, Zomba
+265 995 089 475

Newsletter