Lamulo Lachisanu Ndi Chinayi (9): Usamnamizire Mnzako
Eksodo 20:16
Mawu Otsogolera
Lero tipitiriza kukambirana za Malamulo khumi monga takhalatikuchitira m’miyezi iwiri yapitayi. Lerotikambirana pa za lamulo lachisanu ndi chinayi. Koma tisanayang’ane lamuloli tiyeni tione mfundo izi za malamulo khumi onse.
- Malamulo khumi anali mawu amene anachita kuchokera kwa mwini Mulungu. Sakuyener...