Sermons

Koma Si Monga Mwakufuna Kwanga Koma Chifuniro Chanu Ndithu

Mawu Owerengedwa: Yesaya 53:1-7, Ahebri 10:32-36, Mateyu 26:36-50

Mawu Oyamba

“Ambuye ngati mufuna chikho ichi chindipitirire. Koma si monga mwakufuna kwanga koma chifuniro chanu ndithu.” Yesaya 53
akufotokoza molunjika za kubwera kwa Ambuye Yesu ndi za mazunzo ake. Zimenezi sizinangochitika ayi, zinali zitanenedwa kale ku chipangano chakal...

Read more

 

M’moyo Wa Chikhristu Timakumana Ndi Zofowoka Zambiri

Mawu Oyamba

Mabuku onse a Uthenga wabwino akutsimikiza za kuwuka kwa Ambuye Yesu. Yohane akufotokoza za kuonekera kwa ophunzira ake katatu. Marko akunena kuti anaonekera kanayi koma kwa ophunzira anaonekera katatu. Akutipatsa phunziro kuti ophunzira a Yesi anali osakhazikika kwenikweni Yesu asanakwere kumwamba. Anali ndi chifowoko.

Kutambasula Mawu

Read more

 

The Power Of Christ’s Resurrection And Appearances To Believers

Scriptures: Luke 24: 13-35, John 11: 25-26

The story of Christ’s resurrection is a remarkable turn to the Christian faith. It separates Christianity from all beliefs in that God came to meet the needs of the people. As illustrated in Romans 5:8 that while we were yet sinners, Christ died for us. The story from Luke 24:13-26 draws out four lessons for us Christians.

    ...

    Read more

     

About Us

Zomba CCAP congregation, located in Zomba City, the old capital of Malawi, was established in 1898, and currently boasts 1,638 Christians, of which 115 are church elders and 103 church deacons. It has vibrant women and youth ministries, and a management team that co-ordinates the work of eleven committees, among which are the partnership, evangelism and intercessory, and music committee, as well as faith and works committee... Read more

Announcements & Events

Explosion 2023 Posted: 13 Apr, 2023
Zomba CCAP Holy Week Time Table Posted: 3 Apr, 2023

Address

Zomba C.C.A.P.
Chimbiya Road
P.O. Box 355, Zomba
+265 995 089 475

Newsletter