M’moyo Wa Chikhristu Timakumana Ndi Zofowoka Zambiri
Mawu Oyamba
Mabuku onse a Uthenga wabwino akutsimikiza za kuwuka kwa Ambuye Yesu. Yohane akufotokoza za kuonekera kwa ophunzira ake katatu. Marko akunena kuti anaonekera kanayi koma kwa ophunzira anaonekera katatu. Akutipatsa phunziro kuti ophunzira a Yesi anali osakhazikika kwenikweni Yesu asanakwere kumwamba. Anali ndi chifowoko.
Kutambasula Mawu