Kupulumutsa Ena Pogwiritsa Ntchito Chuma Kapena Zomwe Mulungu Watidalitsa Nazo.
Mabuku: Salimo 1:1-6, Habakuku 1:1-17, Mateyu 14:13-21
Mawu Oyamba
Mulungu akupereka njira zosiyanasiyana kwa aliyense kuti afikire ena kuti enawonso apulumutsidwe. Mwachitsanzo, dzulo Abusa a Masambuka anafotokoza kuti anthu amene anamanga Kachisi wathu wa Zomba CCAP onse anamwalira kalekale koma anagwiritsa nzeru, luso, mphamvu ndi chuma chawo kuti anthu ambiri kuphatikiza...