Tapulumutsidwa Kuti Tikatumikire Ena
Mabuku Owerengedwa: Masalimo 91:1-11, Estere 4:7-17, 1 Akorinto 12:12-20
Mawu Oyamba
Ife Akhrstu ndife anthu opulupumitsidwa chifukwa cha Yesu Khristu. Kubadwa kwake kwa Yesu Khristu ndiko chiyambi cha chipulumutso chathu. Chipulumutso chimenechi chimafika pachimake pamene Yesu anapachikidwa pamtanda nafa, imfa yomwe timakumbukira panyengo ya Pasaka. Chipulumutso chathu chomwe tinachilandira chikuyenera...